T-No - Udani (feat. Maria)

Tazunzika kwa nthawi yayitali ndi udani
Ayaye eh eh, ayaye eh eh
Tazunzika kwa nthawi yayitali ndi udani
Ayaye eh eh, ayaye eh eh
Udani
Udani
Ayaye eh eh, ayaye eh eh
Udani
Udani
Ayaye eh eh, ayaye eh eh
Wagulitsa m'bale wako ngati kapolo Ndi cholinga choti uzitukule pang'ono
Wakaniza udindo nzako ndi ophunzira
Wafuna ntundu wako wokha utapindula
Thangata was a system
The Nguru people were a victim
Atsamunda anali mdani wathu
Pano mzungu amadanidwa ndi anthu yeye
Tazunzika kwa nthawi yayitali ndi udani
Ayaye eh eh, ayaye eh eh
Tazunzika kwa nthawi yayitali ndi udani
Ayaye eh eh, ayaye eh eh
Udani
Udani
Ayaye eh eh, ayaye eh eh
Udani
Udani
Ayaye eh eh, ayaye eh eh
Tazunzika ndi machimo amakolo Pano ndife amene tili akapolo
Koma zinalakwa kale ka
Madzi wotayika samawoleka
Funso ndi loti tipange bwanji?
Udani tidzathetsa tsiku lanji?
Mwina ndiwe Nkhonde
Umadana ndi a Yao
Chifukwa chake sichina
Ndizomwe ankachita makolo awo
Lero uli mu boma
Ukutengeka ndi dyera
Mawa ana ako adzawada
Chifukwa choti iwe sukumvera
Oooooo oooooo oooooo ooo
Oooooo ooooooo ooooo ooo
Ooooo ooo ooo oooo oooo
Oooo oooooo ooooo ooo
Eh heyeye heyehe
Eh heyeye heyehe
Sibabaze hee
Sibabaze
Sibabaze hee
Sibabaze
Sibabaze hee
Sibabaze
Sibabaze hee
Sibabaze
Sibabaze hee
Sibabaze
Sibabaze hee
Sibabaze

Written by:
Edward Chikhwenda

Publisher:
Lyrics © O/B/O DistroKid

Lyrics powered by Lyric Find