T-No - I'm Dependent

Yeah, hahaha,
I feel like Li Wu in this joint....
In the studio preparing to jump on "Pray a lot"...
I feel like The Gosple, Aubrey Mvula right before he jumped on "I'ma do it for ya"...
I'm feeling blessed y'all!
I feel like KB, just when he was about to record "I'ma just do it"....
Hahaha, I depend on God bra! yeah!
Bet you're wondering why I am feeling like a 100 bucks
Jumping up and down all over like a 100 bucks
Man i'm feeling like I now can do some summersaults
Like an acrobatic man can do some summersaults
Ndi Yesu olo n'tagwa ndimagwera m'manja mwake
Satana sindim'patsa mita iye sangamake
Ndinayisova Yesu ndi yankho checka calculator
Opanda ku dalila Yesu ndithu tchimo sungathe kuleka
Ndayesa kusiya tchimo ndekha, nzosatheka
Ndayesa kuyuza nzeru zanga, nzosatheka
Ndayesa kuyuza mphavu zanga, nzosatheka
Olo shasha masamba sangathe, nzosatheka
Koma ndi Yesu khristu zinthu zimatheka
Zinthu zomwe zimavuta kale zimaphweka
Im finding life easier and my secret is
I lean on Jesus Christ who helps me in my weaknesses
(Why you joyous all the time?)
I depend on God
(Confident you'll make it through)
I depend on God
(Can't you see no one has done it?)
I depend on God
(What make's you think you're any different?)
I depend on God
(Awawa simatama)
I'm dependent
(Izizi si mphavu zanga)
I'm dependent
(Opanda Yesu sindingathe)
I'm dependent
(Ndimadalila Yesu yekha)
I'm dependent
I'm dependent on God, ndaponda mwala though
Tawonani ndachira mutu opanda panado
Ok ok, bwino bwino osapanga zanga
Koma ndikachira ndimadziwa kuti si mphavu zanga
Alipo Yesu amene amachiza ma doctor akalephera
2nd Chronicles 16:12 n'zomwe ikunena
Yesu amatha opanda iye ndili chabe ka
Ndi mwazi wake okhawo umene ungandichape ka
Ndaponda mwala, sindida nkhawa, zanga zinayera
I'm dependent on Jehovah osati mayina ena
Ena ndi mafano
Ena ndi ma fana
Ena ndi ma fano ongofuna atafana na
I'm depedent on God, ine pa easy basi
I never worry bout tomorrow zamudziko basi
What I'll eat and what I dress, amapatsa ka
Yehova ndi m'busa wanga ndimangophaka pasture ka
(Why you joyous all the time?)
I depend on God
(Confident you'll make it through)
I depend on God
(Can't you see no one has done it?)
I depend on God
(What make's you think you're any different?)
I depend on God
(Awawa simatama)
I'm dependent
(Izizi si mphavu zanga)
I'm dependent
(Opanda Yesu sindingathe)
I'm dependent
(Ndimadalila Yesu yekha)
I'm dependent
(Why you joyous all the time?)
I depend on God
(Confident you'll make it through)
I depend on God
(Can't you see no one has done it?)
I depend on God
(What make's you think you're any different?)
I depend on God
(Awawa simatama)
I'm dependent
(Izizi si mphavu zanga)
I'm dependent
(Opanda Yesu sindingathe)
I'm dependent
(Ndimadalila Yesu yekha)
I'm dependent

Written by:
Edward Chikhwenda

Publisher:
Lyrics © O/B/O DistroKid

Lyrics powered by Lyric Find